1 Samueli 20:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cifukwa cace ucitire kapolo wako zokoma mtima; popeza wamcititsa kapolo wako kupangana nawe pangano la kwa Yehova; koma ngati mwa ine muli coipa ciri conse, undiphe wekha; udzapita nane bwanji kwa atate wako?

1 Samueli 20

1 Samueli 20:1-18