1 Samueli 18:18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Davide anati kwa Sauli, Ine ndine yani, ndi moyo wanga uli wotani, kapena banja la atate wanga liri lotani m'Israyeli, kuti ine ndidzakhala mkamwini wa mfumu?

1 Samueli 18

1 Samueli 18:8-27