1 Samueli 17:47 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndi msonkhano wonse uno udzazindikira kuti Yehova sapulumutsa ndi lupanga, kapena ndi mkondo; pakuti Yehova ndiye mwini nkhondo, ndipo iye adzakuperekani inu m'manja athu.

1 Samueli 17

1 Samueli 17:42-48