1 Samueli 17:43 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Mfilisti anati kwa Davide, Ine ndine garu kodi, kuti iwe ukudza kwa ine ndi ndodo? Ndi Mfilistiyo anatukwana Davide nachula milungu yace.

1 Samueli 17

1 Samueli 17:36-49