1 Samueli 13:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Samueli anati, Mwacitanji? Nati Sauli, Cifukwa ndinaona kuti anthuwo alinkubalalika kundisiya ine, ndi kuti inu simunafika masiku aja tinapangana, ndi kuti Afilisti anasonkhana ku Mikimasi;

1 Samueli 13

1 Samueli 13:9-18