1 Samueli 11:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Nahasi Mamoni ananena nao, Ndidzapangana nanu, ngati mulola kuti maso a ku dzanja lamanja anu onse akolowoledwe; potero ndidzanyazitsa Aisrayeli onse.

1 Samueli 11

1 Samueli 11:1-7