1 Samueli 10:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Sauli anati kwa mbale wa atate wace, Anatiuza momveka kuti aburuwo anapezedwa kale. Koma sanamdziwitsa mau aja Samueli ananena zaufumuwo.

1 Samueli 10

1 Samueli 10:8-26