1 Samueli 10:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo kunali, kuti onse amene anamdziwiratu kale, pakuona ici cakuti, onani, iye ananenera pamodzi ndi aneneri, anati wina ndi mnzace, Ici nciani cinamgwera mwana wa Kisi? Kodi Saulinso ali mwa aneneri?

1 Samueli 10

1 Samueli 10:4-16