1 Petro 3:20 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

imene inakhala yosamvera kale, pamene kuleza mtima kwa Mulungu kunalindira, m'masiku a Nowa, pokhala m'kukonzeka cingalawa, m'menemo owerengeka, ndiwo amoyo asanu ndi atatu, anapulumutsidwa mwa madzi;

1 Petro 3

1 Petro 3:18-22