1 Petro 2:20 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti mbiri yokoma yanji, mukapirira pocimwa ndi kubwanyulidwapo? Komatu, ngati pocita zabwino, ndi kumvako zowawa mumapirira, kumeneko ndiko cisomo pa Mulungu.

1 Petro 2

1 Petro 2:15-25