1 Petro 1:14-16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

14. monga ana omvera osadzifanizitsanso ndi zilakolako zakale, pokhala osadziwa inu;

15. komatu monga iye wakuitana inu ali woyera mtima, khaiani inunso oyera mtima m'makhalidwe anu onse;

16. popeza kwalembedwa, Muzikhala oyera mtima, pakuti Ine ndine woyera mtima.

1 Petro 1