14. monga ana omvera osadzifanizitsanso ndi zilakolako zakale, pokhala osadziwa inu;
15. komatu monga iye wakuitana inu ali woyera mtima, khaiani inunso oyera mtima m'makhalidwe anu onse;
16. popeza kwalembedwa, Muzikhala oyera mtima, pakuti Ine ndine woyera mtima.