1 Mbiri 9:22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Iwo onse osankhidwa akhale odikira kuzipata ndiwo mazana awiri mphambu khumi ndi awiri. Iwo anawerengedwa monga mwa cibadwidwe cao, m'midzi mwao, amene Davide ndi Samueli mlauli anawaika m'udindo wao.

1 Mbiri 9

1 Mbiri 9:21-30