33. Ndipo Neri anabala Kisi, ndi Kisi anabala Sauli, ndi Sauli anabala Yonatani, ndi Malikisuwa, ndi Abinadabu, ndi Esibaala.
34. Ndi mwana wa Yonatani ndiye Meri-baala; ndi Meri-baala anabala Mika.
35. Ndi ana a Mika: Pitoni, ndi Meleki, ndi Tareya, ndi Ahazi.
36. Ndi Ahazi anabala Yehoada, ndi Yehoada anabala Alemeti, ndi Azimaveti, ndi Zimri; ndi Zimri anabala Moza;
37. ndi Moza anabala Bineya, mwana wace ndiye Rafa, mwana wace Eleasa, mwana wace Azeli;