1 Mbiri 8:33-37 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

33. Ndipo Neri anabala Kisi, ndi Kisi anabala Sauli, ndi Sauli anabala Yonatani, ndi Malikisuwa, ndi Abinadabu, ndi Esibaala.

34. Ndi mwana wa Yonatani ndiye Meri-baala; ndi Meri-baala anabala Mika.

35. Ndi ana a Mika: Pitoni, ndi Meleki, ndi Tareya, ndi Ahazi.

36. Ndi Ahazi anabala Yehoada, ndi Yehoada anabala Alemeti, ndi Azimaveti, ndi Zimri; ndi Zimri anabala Moza;

37. ndi Moza anabala Bineya, mwana wace ndiye Rafa, mwana wace Eleasa, mwana wace Azeli;

1 Mbiri 8