24. ndi Hananiya, ndi Elamu, ndi Antotiya,
25. ndi Ifideya, ndi Penueli, ana a Sasaki;
26. ndi Samserai, ndi Sehariya, ndi Ataliya,
27. ndi Yaaresiya ndi Eliya, ndi Zikiri, ana a Yerohamu.
28. Awa ndi akuru a nyumba za makolo mwa mibadwo yao, ndiwo akuru anakhala m'Yerusalemu awa.