23. ndi Abidoni, ndi Zikiri, ndi Hanani,
24. ndi Hananiya, ndi Elamu, ndi Antotiya,
25. ndi Ifideya, ndi Penueli, ana a Sasaki;
26. ndi Samserai, ndi Sehariya, ndi Ataliya,
27. ndi Yaaresiya ndi Eliya, ndi Zikiri, ana a Yerohamu.
28. Awa ndi akuru a nyumba za makolo mwa mibadwo yao, ndiwo akuru anakhala m'Yerusalemu awa.
29. Ndipo m'Gibeoni anakhala atate a Gibeoni, dzina la mkazi wace ndiye Maaka;
30. ndi mwana wace woyamba ndiye Abidoni, opondana naye ndi Zuri, ndi Kisi, ndi Baala, ndi Nadabu,
31. ndi Gedoro, ndi Ahiyo, ndi Zekeri.