1 Mbiri 8:16-29 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

16. ndi Mikaeli, ndi Isipa, ndi Yoha, ana a Beriya;

17. ndi Zebadiya, ndi Mesulamu, ndi Hiziki, ndi Heberi,

18. ndi Ismerai, ndi Izliya, ndi Yobabu, ana a Elipaala;

19. ndi Yakimu, ndi Zikiri, ndi Zabidi,

20. ndi Elianai, ndi Ziletai, ndi Elieli,

21. ndi Adaya, ndi Beraya, ndi Simirati, ana a Simei;

22. ndi Isipani, ndi Eberi, ndi Elieli,

23. ndi Abidoni, ndi Zikiri, ndi Hanani,

24. ndi Hananiya, ndi Elamu, ndi Antotiya,

25. ndi Ifideya, ndi Penueli, ana a Sasaki;

26. ndi Samserai, ndi Sehariya, ndi Ataliya,

27. ndi Yaaresiya ndi Eliya, ndi Zikiri, ana a Yerohamu.

28. Awa ndi akuru a nyumba za makolo mwa mibadwo yao, ndiwo akuru anakhala m'Yerusalemu awa.

29. Ndipo m'Gibeoni anakhala atate a Gibeoni, dzina la mkazi wace ndiye Maaka;

1 Mbiri 8