16. ndi Mikaeli, ndi Isipa, ndi Yoha, ana a Beriya;
17. ndi Zebadiya, ndi Mesulamu, ndi Hiziki, ndi Heberi,
18. ndi Ismerai, ndi Izliya, ndi Yobabu, ana a Elipaala;
19. ndi Yakimu, ndi Zikiri, ndi Zabidi,
20. ndi Elianai, ndi Ziletai, ndi Elieli,
21. ndi Adaya, ndi Beraya, ndi Simirati, ana a Simei;
22. ndi Isipani, ndi Eberi, ndi Elieli,
23. ndi Abidoni, ndi Zikiri, ndi Hanani,
24. ndi Hananiya, ndi Elamu, ndi Antotiya,
25. ndi Ifideya, ndi Penueli, ana a Sasaki;
26. ndi Samserai, ndi Sehariya, ndi Ataliya,
27. ndi Yaaresiya ndi Eliya, ndi Zikiri, ana a Yerohamu.
28. Awa ndi akuru a nyumba za makolo mwa mibadwo yao, ndiwo akuru anakhala m'Yerusalemu awa.
29. Ndipo m'Gibeoni anakhala atate a Gibeoni, dzina la mkazi wace ndiye Maaka;