1 Mbiri 8:10-22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

10. ndi Yeuzi, ndi Sakiya, ndi Mirima. Awa ndi ana ace akurua nyumbazamakolo ao.

11. Ndi Husimu anambalira Abitubu, ndi Elipaala.

12. Ndi ana a Elipaala: Eberi, ndi Misamu, ndi Semedi, amene anamanga Ono, ndi Ludi ndi miraga yace,

13. ndi Beriya, ndi Sema; ndiwo akuru a nyumba za makolo a iwo okhala m'Ayaloni, amene anathawitsa okhala m'Gati;

14. ndi Ahio, Sasaki, ndi Yeremoti,

15. ndi Zebadiya, ndi Aradi, ndi Ederi,

16. ndi Mikaeli, ndi Isipa, ndi Yoha, ana a Beriya;

17. ndi Zebadiya, ndi Mesulamu, ndi Hiziki, ndi Heberi,

18. ndi Ismerai, ndi Izliya, ndi Yobabu, ana a Elipaala;

19. ndi Yakimu, ndi Zikiri, ndi Zabidi,

20. ndi Elianai, ndi Ziletai, ndi Elieli,

21. ndi Adaya, ndi Beraya, ndi Simirati, ana a Simei;

22. ndi Isipani, ndi Eberi, ndi Elieli,

1 Mbiri 8