10. ndi Yeuzi, ndi Sakiya, ndi Mirima. Awa ndi ana ace akurua nyumbazamakolo ao.
11. Ndi Husimu anambalira Abitubu, ndi Elipaala.
12. Ndi ana a Elipaala: Eberi, ndi Misamu, ndi Semedi, amene anamanga Ono, ndi Ludi ndi miraga yace,
13. ndi Beriya, ndi Sema; ndiwo akuru a nyumba za makolo a iwo okhala m'Ayaloni, amene anathawitsa okhala m'Gati;
14. ndi Ahio, Sasaki, ndi Yeremoti,
15. ndi Zebadiya, ndi Aradi, ndi Ederi,
16. ndi Mikaeli, ndi Isipa, ndi Yoha, ana a Beriya;
17. ndi Zebadiya, ndi Mesulamu, ndi Hiziki, ndi Heberi,
18. ndi Ismerai, ndi Izliya, ndi Yobabu, ana a Elipaala;
19. ndi Yakimu, ndi Zikiri, ndi Zabidi,
20. ndi Elianai, ndi Ziletai, ndi Elieli,
21. ndi Adaya, ndi Beraya, ndi Simirati, ana a Simei;
22. ndi Isipani, ndi Eberi, ndi Elieli,