1 Mbiri 8:1-7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Ndipo Benjamini anabala Bela mwana wace vyoyamba, Asibeli waciwiri, ndi Ahara wacitatu,

2. Noha wacinai, ndi Rafa wacisanu.

3. Ndi Bela anali ndi ana: Adara, ndi Gera, ndi Abihudi,

4. ndi Abisuwa, ndi Namani, ndi Ahowa,

5. ndi Gera, ndi Sefufani, ndi Huramu.

6. Ndi ana a Ehudi ndi awa: ndiwo akuru a nyumba za makolo ao a iwo okhala ku Geba, ndipo anawatenga ndende kumka ku Manahati,

7. natenga ndende Namani, ndi Ahiya, ndi Gera, ndipo, anabala Uza, ndi Ahihudi.

1 Mbiri 8