1 Mbiri 7:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndi pamodzi nao mwa mibadwo yao, mwa nyumba za makolo ao, panali magulu a nkhondo zikwi makumi atatu mphambu zisanu ndi cimodzi, popeza anacuruka akazi ao ndi ana ao.

1 Mbiri 7

1 Mbiri 7:1-8