1 Mbiri 7:31-40 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

31. Ndi ana a Beriya: Heberi, ndi Malikieli, ndiye atate wa Birizaiti.

32. Ndi Heberi anabala Yafteti, ndi Someri, ndi Hotamu, ndi Suwa mlongo wao.

33. Ndi ana a Yafteti: Pasaki, ndi Bimali, ndi Asvati. Awa ndi ana a Yafteti.

34. Ndi ana a Semeri: Ahi, ndi Roga, Yehuba, ndi Aramu.

35. Ndi ana a Helemu mbale wace: Zofa, ndi Imna, ndi Selesi, ndi Amali.

36. Ana a Zofa: Suwa, ndi Harineferi, ndi Sauli, ndi Beri, ndi Imra,

37. Bezeri, ndi Hndi, ndi Sama, ndi Silisa, ndi Itirani, ndi Beera.

38. Ndi ana a Yeteri: Yefune, ndi Pisipa, ndi Ara.

39. Ndi ana a Ula: Ara, ndi Hanieli, ndi Rizya.

40. Awa onse ndiwo ana a Aseri, akuru a nyumba za makolo ao, ngwazi zosankhika ndi zamphamvu, akuru mwa akalonga. Oyesedwa mwa cibadwidwe cao otumikira kunkhondo ndiwo amuna zikwi makumi awiri mphambu zisanu ndi cimodzi.

1 Mbiri 7