1 Mbiri 7:29 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

ndi kumalire a ana a Manase; Beteseani ndi miraga yace, Taanaki ndi miraga yace, Megido ndi miraga yace, Dora ndi miraga yace. M'menemo anakhala ana a Yosefe mwana wa Israyeli.

1 Mbiri 7

1 Mbiri 7:28-38