1 Mbiri 7:26-28 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

26. Ladana mwana wace, Amihudi mwana wace, Elisamu mwana wace,

27. Nuni mwana wace, Yoswa mwana wace.

28. Ndipo dziko lao, ndi pokhala pao ndizo Beteli ndi miraga yace, ndi kum'mawa Narani, ndi kumadzulo Gezeri ndi miraga yace, ndi Sekemu ndi miraga yace, mpaka Aza ndi miraga yace;

1 Mbiri 7