1 Mbiri 7:24 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo mwana wace wamkazi ndiye Seera, amene anamanga Beti-horoni wa kunsi, ndi Beti-horoni wa kumtunda, ndi Uzeniseera.

1 Mbiri 7

1 Mbiri 7:19-28