1 Mbiri 7:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Onsewa ndiwo ana a Yedyaeli; ndiwo akuru a nyumba za makolo ao, ngwazi zamphamvu zikwi khumi mphambu zisanu ndi ziwiri kudza mazana awiri akuturuka kugulu kunkhondo.

1 Mbiri 7

1 Mbiri 7:5-14