43. mwana wa Yabati, mwana wa Gerisomu, mwana wa Levi.
44. Ndi ku dzanja lamanzere abale ao ana a Merari: Etani mwana wa Kisi, mwana wa Abidi, mwana wa Maluki,
45. mwana wa Hasabiya, mwana wa Amaziya, mwana wa Hilikiya,
46. mwana wa Amzi, mwana wa Bani, mwana wa Semeri,