1 Mbiri 6:32 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anatumikira ndi kuyimba pakhomo pa kacisi wa cihema cokomanako mpaka Solomo adamanga nyumba ya Yehova m'Yerusalemu, naimirira m'utumiki wao monga mwa malongosoledwe ao.

1 Mbiri 6

1 Mbiri 6:29-40