1 Mbiri 6:28-31 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

28. Ndi ana a Samueli: woyamba Yoeli, ndi waciwiri Abiya.

29. Ana a Merari: Mali, Libni mwana wace, Simei mwana wace, Uza mwana wace,

30. Simeya mwana wace, Hagiya mwana wace, Asaya mwana wace.

31. Ndipo iwo aja Davide anawaimika a udindo wa nyimbo m'nyumba ya Yehova, litafikira kupumula likasalo, ndi awa.

1 Mbiri 6