1 Mbiri 6:15-27 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

15. ndi Yehozadaki analowa undende muja Yehova anatenga ndende Yuda ndi Yerusalemu ndi dzanja la Nebukadinezara.

16. Ana a Levi: Gerisomu, Kohati ndi Merari.

17. Ndipo maina a ana a Gerisomu ndi awa: Libni, ndi Simei.

18. Ndipo ana a Kohati ndiwo Amramu, ndi lzara, ndi Hebroni, ndi Uzieli.

19. Ana a Merari: Mali ndi Musi. Ndi mabanja a Alevi monga mwa nyumba za makolo ao ndi awa.

20. Wa Gerisomu: Libni mwana wace, Yahati mwana wace, Zina mwana wace,

21. Yowa mwana wace, Ido mwana wace, Zera mwana wace, Yeaterai mwana wace.

22. Ana a Kohati: Aminadabu mwana wace, Kora mwana wace, Asiri mwana wace,

23. Elikana mwana wace, ndi Ebiasafu mwana wace, ndi Asiri mwana wace,

24. Tahati mwana wace, Urieli mwana ware, Uziya mwana wace, ndi Sauli mwana wace.

25. Ndi ana a Elikana: Amasai, ndi Ahimoti.

26. Elikana: ana a Elikana Zofai mwana wace, ndi Nahati mwana wace,

27. Eliabu mwana wace, Yerohamu mwana wace, Elikana mwana wace.

1 Mbiri 6