1. Ana a Levi: Gerisomu, Kohati, ndi Merari.
2. Ndi ana a Kohati: Amramu, Izara, ndi Hebroni, ndi Uzieli.
3. Ndi ana a Amramu: Aroni, ndi Mose, ndi Miriamu. Ndi ana a Aroni: Nadabu, ndi Abihu, Eleazara, ndi Itamara.
4. Eleazara anabala Pinehasi, Pinehasi anabala Abisua,
5. ndi Abisua anabala Buki, ndi Buki anabala Uzi,
6. ndi Uzi anabala Zerahiya, ndi Zerahiya anabala Merayoti,
7. Merayoti anabala Amariya, ndi Amariya anabala Ahitubu,
8. ndi Ahitubu anabala Zadoki, ndi Zadoki anabala Ahimaazi,