1. Ana a Levi: Gerisomu, Kohati, ndi Merari.
2. Ndi ana a Kohati: Amramu, Izara, ndi Hebroni, ndi Uzieli.
3. Ndi ana a Amramu: Aroni, ndi Mose, ndi Miriamu. Ndi ana a Aroni: Nadabu, ndi Abihu, Eleazara, ndi Itamara.
4. Eleazara anabala Pinehasi, Pinehasi anabala Abisua,