3. ana a Rubeni mwana woyamba wa Israyeli: Hanoki, ndi Palu, Hezroni, ndi Karmi.
4. Ana a Yoeli: Semaya mwana wace, Gogi mwana wace, Simei mwana wace,
5. Mika mwana wace, Reaya mwana wace, Baala mwana wace,
6. Beera mwana wace, amene Tigilati Pilesere wa ku Asuri anamtenga ndende; ndiye kalonga wa Arubeni.
7. Ndi abale ace monga mwa mabanja ao, powerenga cibadwidwe ca mibadwo yao: akuru ndiwo Yeyeli, ndi Zekariya,