1 Mbiri 28:18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

ndi ca guwa la nsembe lofukizapo la golidi woyengetsa woyesedwa kulemera kwace, ndi cifaniziro ca gareta wa akerubi agolidi akufunyulula mapiko ao ndi kuphimba likasa la cipangano la Yehova.

1 Mbiri 28

1 Mbiri 28:17-20