21. Wa Rehabiya: wa ana a Rehabiya, mkuru ndi Isiya.
22. Wa Aizari: Selomoti; wa ana a Selomoti, Yahati.
23. Ndi wa ana a Hebroni: mkuru ndi Yeriya, waciwiri Amariya, wacitatu Yahazieli, wacinai Yekameamu.
24. Wa ana a Uziyeli, Mika; wa ana a Mika, Samiri.
25. Mbale wa Mika, Isiya; a ana a Isiya, Zekariya,
26. Ana a Merari: Mali ndi Musi; mwana wa Yaziya, Beno.
27. Ana a Merari: wa Yaziya, Beno, ndi Sohamu, ndi Sakuri, ndi Ibri.
28. Wa Mali: Eleazara, ndiye wopanda ana.
29. Wa Kisi: mwana wa Kisi, Yerameli.