19. Awa ndi malongosoledwe ao m'utumiki wao kulowa m'nyumba ya Yehova, monga mwa ciweruzo adawapatsa Aroni atate wao, monga Yehova Mulungu wa Israyeli anamlamulira.
20. Ndipo wa ana otsala a Levi: wa ana a Amiramu, Subaeli; wa ana a Subaeli, Yedeya.
21. Wa Rehabiya: wa ana a Rehabiya, mkuru ndi Isiya.
22. Wa Aizari: Selomoti; wa ana a Selomoti, Yahati.
23. Ndi wa ana a Hebroni: mkuru ndi Yeriya, waciwiri Amariya, wacitatu Yahazieli, wacinai Yekameamu.
24. Wa ana a Uziyeli, Mika; wa ana a Mika, Samiri.
25. Mbale wa Mika, Isiya; a ana a Isiya, Zekariya,
26. Ana a Merari: Mali ndi Musi; mwana wa Yaziya, Beno.
27. Ana a Merari: wa Yaziya, Beno, ndi Sohamu, ndi Sakuri, ndi Ibri.
28. Wa Mali: Eleazara, ndiye wopanda ana.
29. Wa Kisi: mwana wa Kisi, Yerameli.
30. Ndi ana a Musi: Mali, ndi Ederi, ndi Yerimoti, Awa ndi ana a Alevi monga mwa nyumba za makolo ao.