1 Mbiri 23:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ana a Amiramu: Aroni, ndi Mose; ndipo Aroni anasankhidwa kuti apatule zopatulikitsa, iye ndi ana ace, kosalekeza, kufukiza pamaso pa Yehova, kumtumikira, ndi kudalitsa m'dzina lace kosatha.

1 Mbiri 23

1 Mbiri 23:5-16