1 Mbiri 23:1-2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Atakalamba tsono Davide ndi kucuruka masiku, iye analonga mwana wace Solomo akhale mfumu ya Israyeli.

2. Ndipo anasonkhanitsa akuru onse a Israyeli, ndi ansembe ndi Alevi.

1 Mbiri 23