1 Mbiri 2:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ana a Yuda ndiwo Eri, ndi Onani, ndi Sela; Batisua Mkanani anambalira atatu amenewa. Koma Eri mwana woyamba wa Yuda anali woipa pamaso pa Yehova, ndi iye anamupha.

1 Mbiri 2

1 Mbiri 2:1-11