1 Mbiri 19:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo anamuka ena, namuuza Davide za amunawa. Natumiza iye kukomana nao, pakuti amunawa anacita manyazi kwambiri. Ndipo mfumu inati, Balindani ku Yeriko mpaka zamera ndebvu zanu; zitamera mubwere.

1 Mbiri 19

1 Mbiri 19:1-14