3. Ndipo usiku womwewo mau a Mulungu anadzera Natani, ndi kuti,
4. Kauze Davide mtumiki wanga, Atero Yehova, Usandimangire nyumba yokhalamo;
5. pakuti sindinakhala m'nyumba kuyambira tsiku tija ndinakwera naye Israyeli, kufikira lero Gno; koma wa m'hema m'hema Ine, ndi wa m'kacisi m'kacisi,