1 Mbiri 15:21-23 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

21. ndi Matitiya, ndi Elifelehu, ndi Mikeya, ndi Obedi Edomu, ndi Yeieli, ndi Azaziya, ndi azeze akuyimbira mwa Seminiti, kutsogolera mayimbidwe.

22. Ndi Kenaniya mkuru wa Alevi anayang'anira kusenzako; anawalangiza za kusenza, pakuti anali waluso.

23. Ndi Berekiya ndi Elikana anali odikira likasa.

1 Mbiri 15