1 Mbiri 12:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

ndi Ismaya wa ku Gibeoni, wamphamvu mwa makumi atatuwo ndi woyang'anira makumi atatuwo, ndi Yeremiya, ndi Yahazieli, ndi Yohanani, ndi Yozabadi wa ku Gedera,

1 Mbiri 12

1 Mbiri 12:1-5