1 Mbiri 11:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Anali pamodzi ndi Da vide ku Pasidamimu muja; Afilisti anasonkhanako kunkhondo kumene kunali munda wodzala ndi barele; ndipo anthu anathawa pamaso pa Afilisti.

1 Mbiri 11

1 Mbiri 11:11-14