1 Mbiri 11:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Akuru a amphamvu aja Davide anali nao akulimbika pamodzi naye m'ufumu wace, pamodzi ndi Aisrayeli onse, kumlonga ufumu, monga mwa mau a Yehova akunena za Israyeli, ndi awa.

1 Mbiri 11

1 Mbiri 11:3-15