1 Mbiri 10:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

anauka ngwazi zonse, nacotsa mtembo wa Sauli, ndi mitembo ya ana ace, nabwera nayo ku Yabesi, naika mafupa ao patsinde pa mtengo wathundu ku Yabesi, nasala masiku asanu ndi awiri.

1 Mbiri 10

1 Mbiri 10:9-14