1 Mafumu 8:35 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamene kumwamba kwatsekeka, ndipo kulibe mvula cifukwa ca kucimwira Inu, nakapemphera iwo molunjika kumalo kuno, ndi kubvomereza dzina lanu, ndi kutembenuka kusiya zoipa zao, pakuwasautsa Inu;

1 Mafumu 8

1 Mafumu 8:27-40