1 Mafumu 7:25 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Linasanjikika pa ng'ombe khumi mphambu ziwiri, zitatu zinapenya kumpoto, zitatu kumadzulo, zitatu kumwera, zitatu kum'mawa; ndipo thawalelo linakhazikika pamwamba pa izo; ndipo nkholo zao zinayang'anana.

1 Mafumu 7

1 Mafumu 7:18-26