1 Mafumu 7:20 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo panalinso mitu pamwamba pa nsanamira ziwirizo, pafupi pa mimbayo, inali m'mbali mwace mwa ukondewo; ndipo makangazawo anali mazana awiri, akukhala mizere yozinga nda nda mutu winawo.

1 Mafumu 7

1 Mafumu 7:17-29