1 Mafumu 7:18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

M'mwemo anapanga nsanamira, ndipo panali mizere iwiri yozungulira ukonde umodzi, kukuta ndi makangaza mituyi inali pamwambapo, nacita momwemo ndi mutu winawo.

1 Mafumu 7

1 Mafumu 7:12-20