1 Mafumu 6:9-11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

9. Momwemo anamanga nyumbayo naitsiriza, naika mitanda, naifolera ndi matabwa amikungudza.

10. Ndipo anamanga zipindazo zogundana ndi nyumba yonseyo, cipinda ciri conse msinkhu wace mikono isanu; ndipo anazilumikizitsa kunyumba ndi mitengo yamkungudza.

11. Ndipo mau a Yehova anafika kwa Solomo, nati,

1 Mafumu 6