1 Mafumu 3:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

taona, ndacita monga mwa mau ako; taona ndakupatsa mtima wanzeru ndi wakuzindikira, kotero kuti panalibe wina wolingana ndi iwe kale, ndipo sadzakhalanso wina wolingana ndi iwe utamuka.

1 Mafumu 3

1 Mafumu 3:6-18